GALAMUKANI! Na. 3 2020 | Kodi Tsankho Lidzatha?

Kuti tigonjetse mtima watsankho tiyenera kusintha maganizo athu komanso mmene timaonera zinthu. Werengani magaziniyi kuti muone njira 5 zomwe zingatithandize kuthetsa mtima watsankho.

Kodi Muli Ndi Mtima Watsankho?

Kodi ndi zinthu ziti zomwe zingasonyeze kuti ndife atsankho?

Muzidziwa Zoona Zake

Ngati sitidziwa zolondola, tikhoza kumaona anthu ena molakwika. Onani mmene zinthu zomwe zinachitikira munthu wina yemwe poyamba anali msilikali zikusonyezera mfundo imeneyi.

Muzimvera Ena Chisoni

Kodi kusamvera ena chisoni kumasonyeza chiyani?

Muzizindikira Kuti Ena Amakuposani

Kudzikonda kungachititse kuti munthu akhale watsankho. Koma kodi n’chiyani chomwe chingatithandize kuti tisakhale ndi mtima umenewu?

Muzicheza Ndi Anthu Osiyanasiyana

Onani ubwino wocheza ndi anthu omwe mumasiyana nawo zinthu zina.

Muzisonyeza Chikondi

Chikondi chingatithandize kuthetsa mtima watsankho. Onani zina mwa njira zomwe chikondi chingatithandizire kuchotsa mtima watsankho.

Tsankho Lidzatha

Kodi ndi zinthu 4 ziti zomwe Ufumu wa Mulungu udzachite pothetsa tsankho?

Anasiya Tsankho

Onerani mavidiyo atatu omwe akusonyeza anthu ena omwe anakwanitsa kusiya tsankho.